-
Ezekieli 27:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 Unali kuchita nawo malonda a zovala zokongola kwambiri, malaya akunja opangidwa ndi nsalu yabuluu komanso nsalu yamitundu yosiyanasiyana. Unalinso kuchita nawo malonda a makapeti okhala ndi mitundu iwiri ndiponso zingwe zopota zolimba kwambiri. Unali kuchita nawo malondawo pamalo ako ochitira malonda.
-