-
Ezekieli 40:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 M’lifupi mwa malo owaka miyala am’mbali mwa tinyumba ta zipata munali mofanana ndendende ndi m’litali mwa tinyumbato. Amenewa anali malo owaka miyala a m’munsi.
-