-
Luka 6:42Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
42 Ungauze bwanji m’bale wako kuti, ‘M’bale, taima ndikuchotse kachitsotso kamene kali m’diso lakoka,’ koma iwe osaona mtanda wa denga la nyumba umene uli m’diso lako?+ Wonyenga iwe! Yamba wachotsa mtanda wa denga la nyumba uli m’diso lakowo,+ ndipo ukatero udzatha kuona bwinobwino mmene ungachotsere kachitsotso kamene kali m’diso la m’bale wako.+
-