Luka 17:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Chimodzimodzinso ndi zimene zinachitika m’masiku a Loti.+ M’masiku amenewo anthu anali kudya, kumwa, kugula, kugulitsa, kubzala ndi kumanga. Luka Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 17:28 Yesu—Ndi Njira, ptsa. 218-219 Nsanja ya Olonda,6/15/1989, ptsa. 8-96/1/1988, tsa. 31
28 Chimodzimodzinso ndi zimene zinachitika m’masiku a Loti.+ M’masiku amenewo anthu anali kudya, kumwa, kugula, kugulitsa, kubzala ndi kumanga.