-
Machitidwe 20:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Tsopano ife tinatsogola kukakwera ngalawa n’kuyamba ulendo wopita ku Aso, kumene tinali kukatenga Paulo pangalawa. Iye anatilangiza kuti titsogole, chifukwa anafuna kuyenda wapansi.
-