-
Machitidwe 20:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 M’mawa wake titachoka kumeneko, tinafika pamalo oyang’anana ndi Kiyo. Koma tsiku lotsatira tinaima kwa kanthawi ku Samo, ndipo m’mawa wake tinafika ku Mileto.
-