Aheberi 10:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Komabe, pitirizani kukumbukira masiku akale. Mutalandira kuwala kochokera kwa Mulungu m’masiku amenewo,+ munapirira mayesero aakulu ndi masautso.+ Aheberi Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 10:32 Nsanja ya Olonda,12/15/1999, tsa. 171/1/1998, tsa. 912/1/1996, ptsa. 29-31
32 Komabe, pitirizani kukumbukira masiku akale. Mutalandira kuwala kochokera kwa Mulungu m’masiku amenewo,+ munapirira mayesero aakulu ndi masautso.+