16 Iye anafotokoza zimenezi ngati mmene anachitiranso m’makalata ake onse. Komabe m’makalata akewo muli zinthu zina zovuta kuzimvetsa, zimene anthu osaphunzitsidwa ndi amaganizo osakhazikika akuzipotoza, ngati mmene amachitiranso ndi Malemba ena onse,+ n’kumadziitanira okha chiwonongeko.