Mawu Akumapeto
^ [1] (ndime 9) Werengani Nsanja ya Olonda ya July 15, 2002, tsamba 8 ndi 9 ndiponso mutu 20 m’buku lakuti, Ufumu wa Mulungu Ukulamulira kuti muone zitsanzo za mmene a Mboni za Yehova amasonyezera chikondi kwa abale awo pa nthawi ya mavuto.