Mawu Akumapeto
^ [1] (ndime 4) N’kutheka kuti mwambo wa Pentekosite unkachitika pa nthawi yofanana ndi imene Chilamulo chinaperekedwa m’chipululu cha Sinai. (Eks. 19:1) Ngati zili choncho, ndiye kuti Yesu Khristu anathandiza odzozedwa kuti alowe m’pangano latsopano pa tsiku lofanana ndi limene Mose anathandiza Aisiraeli kulowa m’pangano la Chilamulo.