Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu Akumapeto

^ [1] (ndime 3) Abale ndi alongo athu ena amalephera kusonkhana nthawi zonse chifukwa cha mavuto monga matenda aakulu. Abale ndi alongowa ayenera kudziwa kuti Yehova amamvetsa mavuto awo ndipo amayamikira zimene amayesetsa kuchita pomulambira. Akulu angapeze njira yothandizira abalewa. Mwachitsanzo, angawathandize kuti azimvetsera misonkhano pa foni kapena kuwajambulira kuti amvetsere ali kunyumba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena