Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu Akumapeto

^ [1] (ndime 14) N’zoona kuti pali zambiri zimene zimafanana pakati pa ukapolo wa zaka 70 umene Ayuda anakhala ku Babulo ndi zimene zinachitikira Akhristu odzozedwa. Komabe sitinganene kuti ukapolo wa Ayuda unkaimira zimene zinachitikira Akhristuwa. Choncho si bwino kuganiza kuti chilichonse chimene chinachitika ku ukapolo wa Ayuda chinakwaniritsidwanso pa Akhristu. Pali zina zimene zikusiyana. Mwachitsanzo, ukapolo wa Ayuda unali wa zaka 70 koma wa Akhristu unali wa nthawi yaitali kuposa pamenepa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena