Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

Mawu ake enieni, “pakati pa madzulo awiri.” Malinga n’kunena kwa akatswiri ena, komanso Ayuda achikaraite ndi Asamariya, nthawi imeneyi ikuyambira pamene dzuwa lalowa kufikira pamene mdima weniweni wagwa. Koma Afarisi ndi Arabi ali ndi maganizo osiyana ndi amenewa. Iwo amati, madzulo oyamba ndi pamene dzuwa layamba kupendeka, ndipo madzulo achiwiri ndi kulowa kwa dzuwa kwenikweniko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena