Mawu a M'munsi
Mawu ake enieni, “Ndiyeno kukhala kwa ana a Isiraeli, amene anakhala m’dziko la Iguputo.” Mabaibulo ena akale amasonyeza kuti chiwerengero cha zaka chimene chatchulidwachi sichikuimira zaka zimene Aisiraeli anakhala mu Iguputo mokha ayi, komanso chikuphatikizapo zaka zimene anakhala ku Kanani.