Mawu a M'munsi
Kapena kuti “lolingana ndi sekeli lopatulika.” Umenewu unali muyezo wachikhalire umene anali kuusunga m’chihema chopatulika. N’kutheka kuti mawu akuti “lolingana ndi sekeli la kumalo oyera” anali kungotsindika kuti muyezowo uyenera kukhala wokwanira bwino. Yerekezerani ndi mawu a m’munsi pa 2Sa 14:26.