Mawu a M'munsi
Mawu ake enieni, “Pomatha zaka zitatu, malinga ndi zaka za munthu waganyu.” Nthawi imene munthu waganyu anali kugwira ntchito sanali kuiwonjezera kapena kuichepetsa. Chotero, izi zikutanthauza kuti nthawi ya kutha kwa ulemerero wa Mowabu inali yosasinthika.