Mawu a M'munsi
Mawuwa kwenikweni ndi a pa Zek 11:12, 13. M’nthawi ya Mateyu, buku la Yeremiya linali loyambirira mumpukutu wa mabuku a aneneri. Chotero mwina mabuku onsewo a aneneri, kuphatikizapo la Zekariya, anali kutchedwa kuti Yeremiya. Yerekezani ndi Lu 24:44.