Mawu a M'munsi
a Karl Barth, mmodzi wa ophunzira zaumulungu wotchuka wa chiProtestanti cha m’zana lino, anachitiridwa ripoti kaŵirikaŵiri kukhala akulongosola nthanthi za mnzake wophunzira zaumulungu Paul Tillich kukhala “zonyansa.” Iye samagwirizana molimba ndi wophunzira zaumulungu Rudolf Bultmann, yemwe anakaikira kuwona kwa zolembedwa zina za Baibulo.