Mawu a M'munsi
a Kwa akunja Chikristu chinalozeredwa kukhala “Njira.” “Chinali choyambirira mu Antiokeya [mwinamwake pakati pa zaka 10 ndi 20 pambuyo pake] kuti ophunzira anali mwa chisamaliro chaumulungu anatchedwa Akristu.”—Machitidwe 9:2; 11:26, NW.