Mawu a M'munsi
b “Amuna ogonana ofanana ziŵalo ali ndi unyinji wa mavuto a zamankhwala osiyanasiyana apadera ogwirizanitsidwa choyambirira ku njira yawo ya kugonana.” (Providing Health Care for Gay Men) Pakati pa mavuto a matenda oterowo pali kutaikiridwa kwa chilakolako chakudya, chinzonono cha ku chiŵalo chogonanira ndi kotulutsira zonyansa, kutupa ndi zironda m’malo a m’seri, kulephera kwa ziŵalo zogonanira, ndi nthenda ya Bowen.