Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nzowona kuti Chilamulo cha Mose chinalengeza mkazi wosamba kukhala “wodetsedwa.” (Levitiko 15:19-33) Koma chimenechi chinali kokha m’lingaliro lamwambo. Mwachiwonekere, malamuloŵa anatumikira kuphunzitsa ulemu wa kupatulika kwa mwazi. (Levitiko 17:10-12) Panthaŵi imodzimodziyo, malamulowo anatumikira kukumbutsa mtundu Wachiyuda kuti mtundu wa anthu ngobadwira mu uchimo ndipo umafunikira mombolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena