Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Kwenikweni ansembe ena Achikatolika anamenya nkhondoyo m’magulu ankhondo a Franco. Wansembe wa ku Zafra, Extremadura, anali wotchuka kwambiri kaamba ka nkhalwe yake. Kumbali ina, ansembe oŵerengeka anatsutsa molimba mtima kuphedwa kwa onyumwiridwa kukhala omvera chisoni boma—ndipo chifupifupi munthu mmodzi anaphedwa kaamba ka chifukwa chimenechi. Kadinala Vidal y Barraquer, amene anayesa kusunga uchete mkati mwa nkhondo yonseyo, anakakamizika ndi boma la Franco kukhala m’dziko lachilendo kufikira imfa yake mu 1943.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena