Mawu a M'munsi
b Pansi pa Chilamulo cha Mose, Mulungu anafuna kuti mwamuna amene wanyenga namwali amukwatire. (Eksodo 22:16, 17; Deuteronomo 22:28, 29) Koma lamulo limenelo linatumikira zosoŵa za anthu a Mulungu pansi pa mikhalidwe ya nthaŵi ndi mbadwo umenewo. Ndipo ngakhale nthaŵiyo, ukwati sunali chinthu chotsimikizirika, popeza kuti tateyo akadauletsa.—Onani magazine athu ena Nsanja ya Olonda, November 15, 1989, “Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga.”