Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pansi pa Chilamulo cha Mose, Mulungu anafuna kuti mwamuna amene wanyenga namwali amukwatire. (Eksodo 22:16, 17; Deuteronomo 22:28, 29) Koma lamulo limenelo linatumikira zosoŵa za anthu a Mulungu pansi pa mikhalidwe ya nthaŵi ndi mbadwo umenewo. Ndipo ngakhale nthaŵiyo, ukwati sunali chinthu chotsimikizirika, popeza kuti tateyo akadauletsa.—Onani magazine athu ena Nsanja ya Olonda, November 15, 1989, “Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena