Mawu a M'munsi
a Liwu lotchulira chinthu lakuti “kupwetekwa” (Chihebri, ʼa·sohnʹ) liribe kugwirizana kwachindunji ndi ‘mkazi wapakati’; chotero, kupwetekwako sikulekezera kwa mkazi yekhayo basi koma moyenerera kukaphatikizaponso ‘ana ake’ amene ali m’chibaliro.