Mawu a M'munsi
a Marx, wobadwa kwa makolo Achiyuda mu 1818 mu imene panthaŵiyo inkatchedwa Prussia, anaphunzirira m’Jeremani ndi kugwira ntchito kumeneko monga mtola nkhani; pambuyo pa 1849 anathera nthaŵi yochuluka ya moyo wake m’London, kumene anamwalilira mu 1883.