Mawu a M'munsi
a Nyumba za kholo limodzi zotsogozedwa ndi atate zimachita bwino m’zachuma kuposa zija zotsogozedwa ndi amayi chifukwa chakuti (1) amuna ali ndi mwaŵi wa malipiro apamwamba ndi (2) atate opanda ulamuliro pa ana kaŵirikaŵiri amanyalanyaza alawansi yopatsa akazi awo kapena malipiro alionse ochilikizira ana.