Mawu a M'munsi
a Kale kwambiri wolemba Baibulo wina analemba mwambi wouziridwa womwe umagogomezera phindu la kulingalira pasadakhale koteroko kuti: “Wochenjera awona ngozi nabisala, koma opusa amankabe nalipsidwa nayo.”—Miyambo 22:3, New International Version.