Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kwenikweni, kufufuza kwaposachedwapa kwasonyeza kuti ngakhale achichepere okulirako a m’zaka za kuchiyambiyambi kwa 20 amavutika kwakukulu pamene makolo awo asudzulana. Kusintha kwachiwonekere kwa mikhalidwe ya makolo awo kumaŵadabwitsa, ikusimba motero The New York Times Magazine. Ambiri amaloŵerera m’moyo wazosangulutsa thupi ndi chisembwere, pamene ena amathetsa kupalana ubwenzi kulikonse, ena akumalumbira kuti sadzakwatira konse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena