Mawu a M'munsi
b The New International Dictionary of New Testament Theology limanena kuti mawu Achigiriki otembenuzidwa kukhala “thupi limodzi” pa Mateyu 19:5b ali ndi tanthauzo lapadera monga matembenuzidwe a mawu Achihebri pa Genesis 2:24 ndipo amasonyeza “chigwirizano chotheratu cha mwamuna ndi mkazi chimene sichingaswedwe popanda kuvulaza awo ogwirizana mu icho.”