Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kukambitsirana kwathu kwazikidwa pa chimene Baibulo limachitcha por·neiʹa, kapena chisembwere choipitsitsa chakugonana. (1 Akorinto 6:9; yerekezerani ndi Levitiko 18:6-22.) Ichi chimaphatikizapo mitundu yonse ya mayanjano achisembwere. Machitidwe ena oipa, monga zisonyezero zoipa, kuwonerera ogonana, ndi kuwona zinthu zamaliseche, pamene kuli kwakuti siziri por·neiʹa, zikhozanso kuvulaza malingaliro a mwana.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena