Mawu a M'munsi
a Liwu Lachihebri lakuti da·vaqʹ (“kuphatika”) “liri ndi tanthauzo la kumamatira kwa munthu wina mwachikondi ndi mokhulupirika.” (Theological Wordbook of the Old Testament) M’Chigiriki, ndiliwu lina lotengedwa ku liwu lotanthauza “kumamatiza,” “kulimbitsa,” “kulumikiza pamodzi zolimba.”