Mawu a M'munsi
a Dr. Leon Rosenberg wa pa Yunivesiti ya Johns Hopkins, Baltimore, Maryland, ku U.S.A., anati: “Pamene mwana afika zaka 9, makolo ayenera kuti anayamba kukhala naye pansi ndi kukambitsirana kwa tsatanetsatane ponena za zinthu zakugonana ndi makhalidwe. Pamene ana apeza chidziŵitso chochuluka kwa makolo awo mpamenenso amakhala abwinopo.”