Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Amene anataya unamwali wawo chifukwa cha kugwiriridwa chigololo kapena kugonedwa paubwana angakhale ndi chitonthozo kudziŵa kuti Mulungu amawawonabe kukhala ‘osalakwa ndi owona.’ (Afilipi 2:15) Aliyense amene anachita dama asanapeze chidziŵitso cha malamulo amakhalidwe abwino a Baibulo mofananamo angapeze chitonthozo kudziŵa kuti chifukwa chosonyeza chikhulupiriro m’dipo la Yesu, ‘anasambitsidwa’ pamaso pa Mulungu. (1 Akorinto 6:11) Mkristu amene wagwera m’chisembwere komano walapa mowona mtima ndipo wachira angakhalenso ndi kaimidwe koyera pamaso pa Mulungu. Kaŵirikaŵiri, anzawo amuukwati achikondi, odera nkhaŵa akhala ofunitsitsa kukhululuka m’mikhalidwe imeneyi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena