Mawu a M'munsi
a Maiko ena, monga Jeremani, ali ndi malamulo okhwima ponena za amene ayenera kupereka chithandizo pankhani za malamulo, kusamukira m’dziko, ndi zakukhoma msonkho. Chotero, muyenera kuzipenda zimenezi musanapereke chithandizo chirichonse kwa alendo chakupeza chilolezo chakukhala m’dziko.