Mawu a M'munsi
a Ngati mukuchitiridwa nkhanza ndi kholo chidakwa, mufunikira chithandizo. Ululirani wachikulire amene mumamkhulupirira. Mwachitsanzo, pakati pa Mboni za Yehova, achichepere amakhala aufulu kufikira akulu ampingo kapena Akristu ena okula msinkhu. Chitsogozo chopindulitsa ponena za kuthandiza mikhole yochitiridwa nkhanza chikupezeka mu Galamukani!, wa October 8, 1991.