Mawu a M'munsi
a M’zitaganya zina achichepere kaŵirikaŵiri amaloledwa kumwa zakumwa zoledzeretsa limodzi ndi zakudya. Ngakhale zitatero, makolo amachita mwanzeru kulingalira mwamphamvu za zimene ziri zokomera kwambiri ana awo ndi kusalola chizoloŵezi chofala kutsogoza zosankha zawo zonse.