Mawu a M'munsi
a Uphungu wabwino wochuluka wonena za kukhala kholo logwira mtima uli m’bukhu lakuti Kupangitsa Moyo Wanu wa Banja Kukhala Wachimwamwe, lofalitsidwa ndi Watchtower Bible and Tract Society of New York, Inc., mitu 7 mpaka 9, yakuti “Kukhala ndi Ana—Thayo ndi Mphotho,” “Ntchito Yanu Monga Makolo,” ndi “Kuphunzitsa Ana Kuyambira pa Ukhanda.”