Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Kugwirira chigololo kwa muukwati kumachitika pamene mwamuna amaposa mphamvu mkazi wake ndi kugonana naye mokakamiza. Amuna ena angakhulupirire kuti “ulamuliro” umene mtumwi Paulo akunena kuti mwamuna ali nawo pa thupi la mkazi wake ngwotheratu. Komabe, Paulo anafotokozanso kuti ‘amuna azikonda akazi awo a iwo okha monga ngati matupi a iwo okha.’ Mtumwi Petro akufotokoza kuti amuna ayenera ‘kuchitira mkazi ulemu, monga chotengera chochepa mphamvu.’ Zimenezo sizimasiya mpata wa chiwawa kapena kugonana kokakamiza.—1 Akorinto 7:3-5; Aefeso 5:25, 28, 29; 1 Petro 3:7; Akolose 3:5, 6; 1 Atesalonika 4:3-7.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena