Mawu a M'munsi
a Ulamuliro waufumu wa Yesu Kristu unayamba mu 1914. Kuti mupeze mafokozedwe atsatanetsatane a nkhaniyi, onani mitu 16 mpaka 18 ya buku lakuti Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi, lofalitsidwa mu 1982 ndi Watchtower Bible and Tract Society of New York, Inc.