Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nthaŵi zina kumwerekera m’kulota muli maso kumasonyeza kuti pali vuto limene lilipo. Kufufuza achikulire okhoterera pakuyerekezera zinthu komwerekera kunasonyeza kuti ambiri a iwo ankachitiridwa nkhanza yakumenyedwa kapena kugonedwa pamene anali ana. Kumwerekera m’kulota ali maso kumakhala chipangizo chowathandiza kupirira. Wachichepere amene anachitiridwa nkhanza afunikira kukhala ndi wachikulire wodalirika womuululira zinthu ndi wopezako thandizo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena