Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Wolemba mbiri wa m’zaka za zana loyamba Wachiyuda Joseph ben Matthias (Flavius Josephus) amasimba kuti podzafika nyengo imeneyi, akulu a ansembe a Aisrayeli anali kusankhidwa ndi kuchotsedwa ndi nthumwi za Roma kaŵirikaŵiri kamodzi pachaka. Mumkhalidwe umenewu, malo a mkulu wa ansembe anayamba kukhala ntchito wamba yolipidwa ndalama imene inakopa anthu oipa m’chitaganyacho. The Babylonian Talmud imasanja makhalidwe oipa a ena a akulu a ansembe ameneŵa. (Pesaḥim 57a) Nayonso Talmud imasimba za chikhoterero cha Afarisi pakukonda kwawo chinyengo. (Soṭah 22b)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena