Mawu a M'munsi
c Thayo lofanana nalo laonedwa munthaŵi yathu inonso. Sinzika zonse za German wa Nazi zimene zinaphatizikidwa mwachindunji m’kuchita nkhanza. Komabe, nzika za German zinadziŵa za thayo la chitaganya komabe modzifunira zinasankha kulekerera mikholeyo pachizunzo cha Nazi.