Mawu a M'munsi
a Anthu ochuluka amene amathandiza odwala nthenda zamaganizo amakhulupirira kuti kulangizidwa ndi akatswiri nkofunika kotero kuti muwonjoke m’chizoloŵezi cha kumwerekeracho. Ngati Mkristu asankha njira yochiritsira imene simaombana ndi malamulo a mkhalidwe a Baibulo, imeneyi ndinkhani ya munthu mwini.