Mawu a M'munsi
b Malinga ndi New American Bible Lachikatolika, mbali ya lemba limeneli imati: “Ine pandekha ndinena kwa iwe kuti, ndiwe ‘Thanthwe,’ ndipo pathanthwe ili ndidzamangapo tchalitchi changa . . . Chilichonse chimene unena kuti chamangidwa padziko lapansi chidzamangidwa kumwamba; chilichonse chimene unena kuti chamasulidwa padziko lapansi chidzamasulidwa kumwamba.”—Onani bokosi, patsamba 17.