Mawu a M'munsi
b Nkhaniyi ikunena za kusinthasintha mtima kumene anthu ambiri amakhala nako. Makolo amene amapsinjika maganizo chifukwa cha kuchita tondovi kwambiri, uchidakwa kapena kumwerekera ndi anamgoneka, kapena matenda ena aakulu akuthupi ndi amaganizo angafunikire chithandizo cha dokotala.