Mawu a M'munsi
a Zowonadi, awo amene ali ndi vuto la kadyedwe sangasale chakudya. Komabe, akhoza kuleka kugwiritsira ntchito chakudya monga chosinthira mzimu wawo. Njira zodyera chakudya mopambanitsa, kudzipha ndi njala, kudzisanzitsa kapena kudzitsegula m’mimba, ndi kuganiza mopambanitsa ponena za chakudya kungaloŵedwe mmalo ndi kadyedwe koyenera.