Mawu a M'munsi
a ORT imapatsa ana madzi, mchere, ndi shuga zofunikira kulimbana ndi nthenda ya kupaza yochepetsa madzi m’thupi. World Health Organization inachitira lipoti mu 1990 kuti pakali pano miyoyo yoposa pa miliyoni imodzi ikupulumutsidwa chaka chilichonse ndi chithandizo chimenechi. Kuti mupeze nsonga zowonjezereka, onani Awake! ya September 22, 1985, masamba 23-5.