Mawu a M'munsi
a Matchulidwe a maphunziro amasiyana m’maiko. M’nkhani zino “sukulu ya sekondale” ikuimira maphunziro okwanira ofunidwa mwalamulo. Mainawo “koleji,” “yunivesite,” “sukulu yophunzitsa maluso a manja,” ndi “sukulu yophunzitsa ntchito” akusonya ku mitundu ya maphunziro owonjezera amene samafunidwa mwalamulo koma amaphunziridwa modzifunira.