Mawu a M'munsi
c Kugona ana mwachionekere kunachititsa mathanyula kufala m’Greece wakale. Anthu ambiri ankatcha achikulire ogona anyamata “mimbulu”—“chizindikiro cha umbombo ndi kulusa kwauchinyama.” Achichepere amene anali kugonedwa ndi iwo anali kutchedwa “ana a nkhosa.”