Mawu a M'munsi
a Nthenda zisanu ndi imodzi ndizo diphtheria, chikuku, polio, tetanus, TB, ndi chifuŵa. WHO ikunena kuti hepatitis B nayonso, imene imapha anthu ambiri kuposa amene AIDS tsopano ikupha, iphatikizidwe m’programu ya katemera.
a Nthenda zisanu ndi imodzi ndizo diphtheria, chikuku, polio, tetanus, TB, ndi chifuŵa. WHO ikunena kuti hepatitis B nayonso, imene imapha anthu ambiri kuposa amene AIDS tsopano ikupha, iphatikizidwe m’programu ya katemera.